Aefeso 5:15 - Buku Lopatulika15 Potero, penyani bwino umo muyendera, si monga opanda nzeru, koma monga anzeru; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Potero, penyani bwino umo muyendera, si monga opanda nzeru, koma monga anzeru; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Samalirani bwino mayendedwe anu. Musayende monga anthu opanda nzeru, koma monga anthu anzeru. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Samalani makhalidwe anu, musakhale ngati opanda nzeru koma ngati anzeru. Onani mutuwo |