Aefeso 4:9 - Buku Lopatulika9 Koma ichi, chakuti, Anakwera, nchiyani nanga koma kuti anatsikiranso ku madera a kunsi kwa dziko? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Koma ichi, chakuti, Anakwera, nchiyani nanga koma kuti anatsikiranso ku madera a kunsi kwa dziko? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Tsono mau akuti “adakwera” tanthauzo lake nchiyani? Ndiye kuti poyamba adaatsikira pansi penipeni pa dziko. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Kodi mawu akuti, “Iye anakwera” akutanthauza chiyani, ngati Iyeyo sanatsikire kunsi kwa dziko lapansi? Onani mutuwo |