Aefeso 4:8 - Buku Lopatulika8 Chifukwa chake anena, M'mene anakwera kumwamba, anamanga ndende undende, naninkha zaufulu kwa anthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Chifukwa chake anena, M'mene anakwera kumwamba, anamanga ndende undende, naninkha zaufulu kwa anthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Paja mau a Mulungu akuti, “Pamene adakwera Kumwamba, adatenga chigulu cha am'ndende, ndipo adagaŵira anthu mphatso.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Nʼchifukwa chake akunena kuti, “Iye atakwera kumwamba, anatenga chigulu cha a mʼndende ndipo anapereka mphatso kwa anthu.” Onani mutuwo |