Aefeso 4:23 - Buku Lopatulika23 koma kuti mukonzeke, mukhale atsopano mu mzimu wa mtima wanu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 koma kuti mukonzeke, mukhale atsopano mu mzimu wa mtima wanu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Mtima wanu, umene uli gwero la maganizo anu, usanduke watsopano. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 kuti mukonzedwe mwatsopano mʼmitima mwanu; Onani mutuwo |