Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Aefeso 4:23 - Buku Lopatulika

23 koma kuti mukonzeke, mukhale atsopano mu mzimu wa mtima wanu,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 koma kuti mukonzeke, mukhale atsopano mu mzimu wa mtima wanu,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Mtima wanu, umene uli gwero la maganizo anu, usanduke watsopano.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 kuti mukonzedwe mwatsopano mʼmitima mwanu;

Onani mutuwo Koperani




Aefeso 4:23
11 Mawu Ofanana  

Mundilengere mtima woyera, Mulungu; mukonze mzimu wokhazikika m'kati mwanga.


Ndipo ndidzawapatsa mtima umodzi, ndi kuika mzimu watsopano m'kati mwao; ndipo ndidzawachotsera mtima wamwala m'thupi mwao, ndi kuwapatsa mtima wamnofu;


Tayani, ndi kudzichotsera zolakwa zanu zonse zimene munalakwa nazo, ndi kudzifunira mtima watsopano, ndi mzimu watsopano; pakuti mudzaferanji inu, nyumba ya Israele?


Ndipo ndidzakupatsani mtima watsopano, ndi kulonga m'kati mwanu mzimu watsopano; ndipo ndidzachotsa mtima wamwala m'thupi, ndi kukupatsani mtima wamnofu.


Ndipo musafanizidwe ndi makhalidwe a pansi pano: koma mukhale osandulika, mwa kukonzanso kwa mtima wanu, kuti mukazindikire chimene chili chifuniro cha Mulungu, chabwino, ndi chokondweretsa, ndi changwiro.


Chifukwa chake tinaikidwa m'manda pamodzi ndi Iye mwa ubatizo kulowa muimfa; kuti monga Khristu anaukitsidwa kwa akufa mwa ulemerero wa Atate, chotero ifenso tikayende m'moyo watsopano.


pakuti chisamaliro cha thupi chili imfa; koma chisamaliro cha mzimu chili moyo ndi mtendere.


Pakuti ife ndife chipango chake, olengedwa mwa Khristu Yesu, kuchita ntchito zabwino, zimene Mulungu anazipangiratu, kuti tikayende m'menemo.


ndipo munavala watsopano, amene alikukonzeka watsopano, kuti akhale nacho chizindikiritso, monga mwa chifaniziro cha Iye amene anamlenga iye;


zosati zochokera m'ntchito za m'chilungamo, zimene tidazichita ife, komatu monga mwa chifundo chake anatipulumutsa ife, mwa kutsuka kwa kubadwanso ndi makonzedwe a Mzimu Woyera,


Mwa ichi, podzimanga m'chuuno, kunena za mtima wanu, mukhale odzisunga, nimuyembekeze konsekonse chisomo chilikutengedwa kudza nacho kwa inu m'vumbulutso la Yesu Khristu;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa