Aefeso 4:21 - Buku Lopatulika21 ngatitu mudamva Iye, ndipo munaphunzitsidwa mwa Iye, monga choonadi chili mwa Yesu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 ngatitu mudamva Iye, ndipo munaphunzitsidwa mwa Iye, monga choonadi chili mwa Yesu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 ngatitu mudamva za Iyeyo, ngatinso mudaphunzitsidwa za Iye, motsata choona chimene chili mwa Yesu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Zoonadi munamva za Iye ndipo munaphunzitsidwa mwa Iye molingana ndi choonadi chimene chili mwa Yesu. Onani mutuwo |