Aefeso 3:4 - Buku Lopatulika4 chimene mukhoza kuzindikira nacho, pakuchiwerenga, chidziwitso changa m'chinsinsi cha Khristu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 chimene mukhoza kuzindikira nacho, pakuchiwerenga, chidziwitso changa m'chinsinsi cha Khristu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Pamene muŵerenga zimenezi, mungathe kuwona kuti ndikumvetsetsadi chinsinsi chonena za Khristu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Pamene mukuwerenga izi, inu mudzazindikira za chidziwitso changa pa chinsinsi cha Khristu, Onani mutuwo |