Aefeso 3:5 - Buku Lopatulika5 chimene sanachizindikiritse ana a anthu m'mibadwo ina, monga anachivumbulutsa tsopano kwa atumwi ndi aneneri ake oyera mwa Mzimu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 chimene sanachizindikiritsa ana a anthu m'mibadwo ina, monga anachivumbulutsa tsopano kwa atumwi ndi aneneri ake oyera mwa Mzimu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Chinsinsi chimenechi anthu a mibadwo yakale sadachidziŵe, koma Mulungu wachiwulula tsopano mwa Mzimu Woyera kwa atumwi ake oyera mtima, ndiponso kwa aneneri ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 chimene sichinawululidwe kwa anthu amibado ina monga momwe tsopano chawululidwa ndi Mzimu wa Mulungu mwa atumwi oyera ndi aneneri. Onani mutuwo |