Aefeso 3:2 - Buku Lopatulika2 ngatitu munamva za udindo wa chisomo cha Mulungu chimene anandipatsa ine cha kwa inu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 ngatitu munamva za udindo wa chisomo cha Mulungu chimene anandipatsa ine cha kwa inu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Kumva mudamva za ntchito imene mwa ufulu wake Mulungu adandipatsa, yolalika pakati panu za kukoma mtima kwake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndithudi, inu munamva za ntchito yachisomo cha Mulungu imene anandipatsa chifukwa cha inu, Onani mutuwo |