Aefeso 3:1 - Buku Lopatulika1 Chifukwa cha ichi ine Paulo, ndine wandende wa Khristu Yesu chifukwa cha inu amitundu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Chifukwa cha ichi ine Paulo, ndine wandende wa Khristu Yesu chifukwa cha inu amitundu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Nchifukwa chake ine Paulo ndimakupemphererani. Ndine womangidwa m'ndende chifukwa chotumikira Khristu ndi kugwirira ntchito inu amene simuli Ayuda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Nʼchifukwa chake ine Paulo, ndili wamʼndende wa Khristu Yesu chifukwa cha inu anthu a mitundu ina. Onani mutuwo |