Aefeso 2:22 - Buku Lopatulika22 chimene inunso mumangidwamo pamodzi, mukhale chokhalamo Mulungu mwa Mzimu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 chimene inunso mumangidwamo pamodzi, mukhale chokhalamo Mulungu mwa Mzimu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Mwa Iyeyu inunso mukumangidwa pamodzi ndi ena onse, kuti mukhale nyumba yokhalamo Mulungu mwa Mzimu Woyera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Ndipo mwa Iye, inunso mukamangidwa pamodzi ndi ena onse kukhala nyumba yokhalamo imene Mulungu amakhala mwa Mzimu wake. Onani mutuwo |