Aefeso 2:21 - Buku Lopatulika21 mwa Iye chimango chonse cholumikizika pamodzi bwino, chikula, chikhale Kachisi wopatulika mwa Ambuye; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 mwa Iye chimango chonse cholumikizika pamodzi bwino, chikula, chikhale Kachisi wopatulika mwa Ambuye; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Mwa Iyeyu nyumba yonse ikumangidwa molimba, ndipo ikukula kuti ikhale nyumba yopatulika ya Ambuye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Mwa Iyeyo, nyumba yonse yalumikizidwa pamodzi ndipo yakwezedwa kukhala Nyumba yoyera mwa Ambuye. Onani mutuwo |