Aefeso 2:20 - Buku Lopatulika20 omangika pa maziko a atumwi ndi aneneri, pali Khristu Yesu mwini, mwala wa pangodya; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 omangika pa maziko a atumwi ndi aneneri, pali Khristu Yesu mwini, mwala wa pangodya; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Ndinu omangidwa pamodzi m'nyumba yomangidwa pa maziko amene ndi atumwi ndi aneneri, ndipo Khristu Yesu mwini ndiye mwala wapangodya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Ndinu okhazikika pa maziko a atumwi ndi a aneneri, pamodzi ndi Khristu Yesu mwini ngati mwala wa pa ngodya. Onani mutuwo |