Aefeso 3:15 - Buku Lopatulika15 amene kuchokera kwa Iye fuko lonse la m'mwamba ndi la padziko alitcha dzina, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 amene kuchokera kwa Iye fuko lonse la m'mwamba ndi la padziko alitcha dzina, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 amene banja lililonse Kumwamba ndi pansi pano limatchulidwa ndi dzina lao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 amene banja lililonse kumwamba ndi pa dziko lapansi limatchulidwa ndi dzina lawo. Onani mutuwo |