Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Aefeso 3:15 - Buku Lopatulika

15 amene kuchokera kwa Iye fuko lonse la m'mwamba ndi la padziko alitcha dzina,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 amene kuchokera kwa Iye fuko lonse la m'mwamba ndi la padziko alitcha dzina,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 amene banja lililonse Kumwamba ndi pansi pano limatchulidwa ndi dzina lao.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 amene banja lililonse kumwamba ndi pa dziko lapansi limatchulidwa ndi dzina lawo.

Onani mutuwo Koperani




Aefeso 3:15
13 Mawu Ofanana  

Ndipo mudzasiya dzina lanu likhale chitemberero kwa osankhidwa anga, ndipo Ambuye Yehova adzakupha iwe, nadzatcha atumiki ake dzina lina;


Masiku omwewo Yuda adzapulumutsidwa, ndi Yerusalemu adzakhala mokhulupirika; ili ndi dzina adzatchedwa nalo, Yehova ndiye chilungamo chathu.


ndipo m'mene anampeza, anadza naye ku Antiokeya. Ndipo kunali, kuti chaka chonse anasonkhana pamodzi mu Mpingo, naphunzitsa anthu aunyinji; ndipo ophunzira anayamba kutchedwa Akhristu ku Antiokeya.


kuti pa makonzedwe a makwaniridwe a nyengozo, akasonkhanitse pamodzi zonse mwa Khristu, za kumwamba, ndi za padziko.


pamwamba pa ukulu wonse, ndi ulamuliro, ndi mphamvu, ndi ufumu, ndi dzina lililonse lotchedwa, si m'nyengo ino ya pansi pano yokha, komanso mwa iyo ikudza;


Chifukwa cha ichi ndipinda maondo anga kwa Atate,


kuti monga mwa chuma cha ulemerero wake akulimbikitseni inu ndi mphamvu mwa Mzimu wake, m'kati mwanu,


mwa Iyenso kuyanjanitsa zinthu zonse kwa Iye mwini, atachita mtendere mwa mwazi wa mtanda wake; mwa Iyetu, kapena za padziko, kapena za mu Mwamba.


Iye wakukhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo. Kwa iye wopambana, ndidzampatsa mana obisika, ndipo ndidzampatsa mwala woyera, ndi pamwalawo dzina latsopano lolembedwapo, wosalidziwa munthu aliyense koma iye wakuulandira.


Iye wakupambana, ndidzamyesa iye mzati wa mu Kachisi wa Mulungu wanga, ndipo kutuluka sadzatulukamonso; ndipo ndidzalemba pa iye dzina la Mulungu wanga, ndi dzina la mzinda wa Mulungu wanga, la Yerusalemu watsopano, wotsika mu Mwamba, kuchokera kwa Mulungu wanga; ndi dzina langa latsopano.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa