Aefeso 3:14 - Buku Lopatulika14 Chifukwa cha ichi ndipinda maondo anga kwa Atate, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Chifukwa cha ichi ndipinda maondo anga kwa Atate, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Nchifukwa chake tsono ndikugwadira Atate, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Nʼchifukwa chake ine ndikugwada pamaso pa Atate, Onani mutuwo |