Aefeso 3:16 - Buku Lopatulika16 kuti monga mwa chuma cha ulemerero wake akulimbikitseni inu ndi mphamvu mwa Mzimu wake, m'kati mwanu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 kuti monga mwa chuma cha ulemerero wake akulimbikitseni inu ndi mphamvu mwa Mzimu wake, m'kati mwanu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Ndikupempha Mulungu kuti kuchokera m'chuma cha ulemerero wake akupatseni mphamvu, ndipo mwa Mzimu wake Woyera alimbitse moyo wanu wauzimu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Ndikupemphera kuti kuchokera mʼchuma cha ulemerero wake alimbikitse moyo wanu wa mʼkati ndi mphamvu za Mzimu wake, Onani mutuwo |