Aefeso 2:6 - Buku Lopatulika6 ndipo anatiukitsa pamodzi, natikhazikitsa pamodzi m'zakumwamba mwa Khristu Yesu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 ndipo anatiukitsa pamodzi, natikhazikitsa pamodzi m'zakumwamba mwa Khristu Yesu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Popeza kuti tili mwa Khristu Yesu, Mulungu adachita ngati kutiwukitsa kwa akufa pamodzi naye, kuti choncho atipatse malo aulemu pamodzi naye m'dziko la Kumwamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ndipo Mulungu anatiukitsa pamodzi ndi Khristu ndi kutikhazika pamodzi ndi Iye mmwamba mwa Khristu Yesu, Onani mutuwo |