Aefeso 2:5 - Buku Lopatulika5 tingakhale tinali akufa m'zolakwa zathu, anatipatsa moyo pamodzi ndi Khristu (muli opulumutsidwa ndi chisomo), Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 tingakhale tinali akufa m'zolakwa zathu, anatipatsa moyo pamodzi ndi Khristu (muli opulumutsidwa ndi chisomo), Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Motero, pamene tinali akufa chifukwa cha machimo athu, Iye adatipatsa moyo pamodzi ndi Khristu. Kukoma mtima kwa Mulungu ndi kumene kudakupulumutsani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 anatipanga kukhala amoyo ndi Khristu ngakhale pamene ife tinali akufa mu zolakwa zathu. Koma tinapulumutsidwa mwachisomo. Onani mutuwo |