Aefeso 1:6 - Buku Lopatulika6 kuti uyamikidwe ulemerero wa chisomo chake, chimene anatichitira ife kwaufulu mwa Wokondedwayo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 kuti uyamikidwe ulemerero wa chisomo chake, chimene anatichitira ife kwaufulu mwa Wokondedwayo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Adaafuna kuti tizitamanda ulemu wake chifukwa adatikomera mtima kopambana, pakutipatsa Mwana wake wokondedwa ngati mphatso yaulere. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Anachita zimenezi kuti tiziyamika ulemerero wa chisomo chake, umene watipatsa kwaulere mwa Khristu amene amamukonda. Onani mutuwo |