Aefeso 1:5 - Buku Lopatulika5 Anatikonzeratu tilandiridwe ngati ana a Iye yekha mwa Yesu Khristu, monga umo kunakomera chifuniro chake, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Anatikonzeratu tilandiridwe ngati ana a Iye yekha mwa Yesu Khristu, monga umo kunakomera chifuniro chake, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Chifukwa chotikonda, adakonzeratu kuti mwa Yesu Khristu atilandire ngati ana ake. Adachita zimenezi chifukwa adaafuna kutero mwa kukoma mtima kwake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Iye anakonzeratu kuti ife titengedwe ngati ana mwa Yesu Khristu, molingana ndi kukonda kwake ndi chifuniro chake. Onani mutuwo |