Aefeso 1:7 - Buku Lopatulika7 Tili ndi maomboledwe mwa mwazi wake, chikhululukiro cha zochimwa, monga mwa kulemera kwa chisomo chake, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Tili ndi maomboledwe mwa mwazi wake, chikhululukiro cha zochimwa, monga mwa kulemera kwa chisomo chake, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Ndi imfa ya Mwana wakeyo Mulungu adatipulumutsa, adatikhululukira machimo athu. Nzazikuludi mphatso zaulere Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Mwa Yesu Khristu, chifukwa cha magazi ake, ife tinawomboledwa ndi kukhululukidwa machimo athu molingana ndi kuchuluka kwa chisomo cha Mulungu Onani mutuwo |