3 Yohane 1:7 - Buku Lopatulika7 pakuti chifukwa cha dzinali anatuluka, osalandira kanthu kwa amitundu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 pakuti chifukwa cha dzinali anatuluka, osalandira kanthu kwa amitundu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Paja adaanyamuka ulendo wao chifukwa cha dzina la Khristu, osalandira thandizo kwa akunja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Pakuti ananyamuka ulendo wawo chifukwa cha dzina la Ambuye, osalandira thandizo kwa osakhulupirira. Onani mutuwo |