3 Yohane 1:6 - Buku Lopatulika6 amene anachita umboni za chikondi chako pamaso pa Mpingo; ngati uwaperekeza amenewo pa ulendo wao koyenera Mulungu, udzachita bwino: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 amene anachita umboni za chikondi chako pamaso pa Mpingo; ngati uwaperekeza amenewo pa ulendo wao koyenera Mulungu, udzachita bwino: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Iwo adachitira umboni chikondi chako pamaso pa mpingo. Ndi bwinodi kuti uŵathandize mokondweretsa Mulungu kupitiriza ulendo wao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Iwo anafotokozera mpingo za chikondi chako. Chonde uwathandize kupitiriza ulendo mʼnjira yokondweretsa Mulungu. Onani mutuwo |