3 Yohane 1:14 - Buku Lopatulika14 koma ndiyembekeza kukuona iwe msanga, ndipo tidzalankhula popenyana. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 koma ndiyembekeza kukuona iwe msanga, ndipo tidzalankhula popenyana. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Ndikuyembekeza kudzakuwona posachedwa. Pamenepo tidzakambirana pakamwa mpakamwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Ndiyembekezera kufika kwanuko posachedwapa, ndipo tidzakambirana pamaso ndi pamaso. Onani mutuwo |