3 Yohane 1:1 - Buku Lopatulika1 Mkuluyo kwa Gayo wokondedwayo, amene ndikondana naye m'choonadi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Mkuluyo kwa Gayo wokondedwayo, amene ndikondana naye m'choonadi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Ine mkulune ndikulemba kalatayi kwa Gayo wokondedwa, amene ndimamkonda kwenikweni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Ndine mkulu wampingo, kulembera: Gayo mnzanga wokondedwa, amene ndimamukonda mʼchoonadi. Onani mutuwo |