2 Yohane 1:3 - Buku Lopatulika3 Chisomo, chifundo, mtendere zikhale ndi ife zochokera kwa Mulungu Atate, ndi kwa Yesu Khristu Mwana wa Atate, m'choonadi ndi m'chikondi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Chisomo, chifundo, mtendere zikhale ndi ife zochokera kwa Mulungu Atate, ndi kwa Yesu Khristu Mwana wa Atate, m'choonadi ndi m'chikondi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Mulungu Atate ndi Yesu Khristu, Mwana wa Atate, atikomere mtima ndi kutipatsa chifundo ndi mtendere m'choona ndi m'chikondi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Chisomo, chifundo ndi mtendere zochokera kwa Mulungu Atate ndi kwa Yesu Khristu, Mwana wa Atate, zikhale ndi ife mʼchoonadi ndi mʼchikondi. Onani mutuwo |