2 Yohane 1:4 - Buku Lopatulika4 Ndakondwera kwakukulu kuti ndapeza ena a ana anu alikuyenda m'choonadi, monga tinalandira lamulo lochokera kwa Atate. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndakondwera kwakukulu kuti ndapeza ena a ana anu alikuyenda m'choonadi, monga tinalandira lamulo lochokera kwa Atate. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ndidakondwera kwambiri kuti ndidapeza ana anu ena akuyenda motsata choona, monga Atate adatilamulira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ndinakondwera kwambiri nditapeza ana anu ena akuyenda mʼchoonadi, monga Atate anatilamulira. Onani mutuwo |