2 Timoteyo 4:6 - Buku Lopatulika6 Pakuti ndilimkuthiridwa nsembe tsopano, ndipo nthawi ya kumasuka kwanga yafika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Pakuti ndilimkuthiridwa nsembe tsopano, ndipo nthawi ya kumasuka kwanga yafika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Paja ine ndiye moyo wanga wayamba kale kuthiridwa ngati nsembe, ndipo nthaŵi yafika kuti ndinyamuke ulendo wanga wochoka m'moyo uno. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Pakuti moyo wanga wayamba kale kuthiridwa ngati nsembe, ndipo nthawi yakwana yoti ndinyamuke ulendo wanga. Onani mutuwo |