2 Timoteyo 4:5 - Buku Lopatulika5 Koma iwe, khala maso m'zonse, imva zowawa, chita ntchito ya mlaliki wa Uthenga Wabwino, kwaniritsa utumiki wako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Koma iwe, khala maso m'zonse, imva zowawa, chita ntchito ya mlaliki wa Uthenga Wabwino, kwaniritsa utumiki wako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Koma iwe, uzikhala maso pa zonse, pirira pa zoŵaŵa, gwira ntchito yolalika Uthenga Wabwino. Kwaniritsa udindo wako mosamala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Koma iwe, khala tcheru nthawi zonse, pirira mʼzovuta, gwira ntchito ya mlaliki, gwira ntchito zonse za utumiki wako. Onani mutuwo |