2 Timoteyo 4:7 - Buku Lopatulika7 Ndalimbana nako kulimbana kwabwino, ndatsiriza njirayo, ndasunga chikhulupiriro: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndalimbana nako kulimbana kwabwino, ndatsiriza njirayo, ndasunga chikhulupiriro: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Ndamenya nkhondo yabwino, ndatsiriza bwino mpikisano wa liŵiro, ndasunga chikhulupiriro. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ndamenya nkhondo yabwino, ndatsiriza bwino mpikisano wa liwiro ndipo ndasunga chikhulupiriro. Onani mutuwo |