2 Timoteyo 2:5 - Buku Lopatulika5 Koma ngatinso wina ayesana nao m'makani amasewero, samveka korona ngati sanayesane monga adapangana. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Koma ngatinso wina ayesana nao m'makani amasewero, samveka korona ngati sanayesana monga adapangana. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Munthu wothamanga pa mpikisano wa liŵiro, sangalandire mphotho ngati sathamanga motsata malamulo a mpikisanowo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Chimodzimodzinso, munthu amene ali pa mpikisano waliwiro, salandira mphotho ya wopambana pokhapokha atatsiriza monga mwa malamulo a mpikisanowo. Onani mutuwo |