2 Timoteyo 1:6 - Buku Lopatulika6 Chifukwa chake ndikukumbutsa iwe ukoleze mphatso ya Mulungu, ili mwa iwe mwa kuika kwa manja anga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Chifukwa chake ndikukumbutsa iwe ukoleze mphatso ya Mulungu, ili mwa iwe mwa kuika kwa manja anga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Nchifukwa chake ndikukukumbutsa kuti mphatso imene Mulungu adakupatsa pamene ndidakusanjika manja, uiyatsenso ngati moto. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Nʼchifukwa chake ndikukukumbutsa kuti upemerere monga amachitira moto, mphatso imene Mulungu anakupatsa nditakusanjika manja. Onani mutuwo |