2 Timoteyo 1:7 - Buku Lopatulika7 Pakuti Mulungu sanatipatse mzimu wa mantha; komatu wa mphamvu ndi chikondi ndi chidziletso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Pakuti Mulungu sanatipatsa mzimu wa mantha; komatu wa mphamvu ndi chikondi ndi chidziletso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Paja Mzimu amene Mulungu adatipatsa, si Mzimu wotipatsa mtima wa mantha ai, koma Mzimu wotipatsa mphamvu, chikondi ndi kudzigwira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Pakuti Mzimu amene Mulungu anatipatsa, si Mzimu wotipatsa manyazi, koma Mzimu wotipatsa mphamvu, chikondi ndi kudzisunga. Onani mutuwo |