2 Timoteyo 1:4 - Buku Lopatulika4 pokhumba usiku ndi usana kukuona iwe, ndi kukumbukira misozi yako, kuti ndidzazidwe nacho chimwemwe; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 pokhumba usiku ndi usana kukuona iwe, ndi kukumbukira misozi yako, kuti ndidzazidwe nacho chimwemwe; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ndikamakumbukira misozi yako, ndimafunitsitsa kukuwona, kuti ndikhale ndi chimwemwe chodzaza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ndikamakumbukira misozi yako, ndimalakalaka nditakuona kuti ndidzazidwe ndi chimwemwe. Onani mutuwo |