2 Samueli 8:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo Yowabu mwana wa Zeruya anayang'anira ankhondo, ndi Yehosafati mwana wa Ahiludi anali wolemba mbiri, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo Yowabu mwana wa Zeruya anayang'anira ankhondo, ndi Yehosafati mwana wa Ahiludi anali wolemba mbiri, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Tsono Yowabu, mwana wa Zeruya, anali mtsogoleri wa ankhondo, ndipo Yehosafati, mwana wa Ahiludi, anali mlembi wolemba mbiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Yowabu mwana wa Zeruya anali mkulu wa ankhondo; Yehosafati mwana wa Ahiludi anali mlembi wa zochitika. Onani mutuwo |