2 Samueli 8:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo Davide anakhala mfumu ya Aisraele onse, Davide naweruza ndi chilungamo milandu ya anthu onse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo Davide anakhala mfumu ya Aisraele onse, Davide naweruza ndi chilungamo milandu ya anthu onse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Motero Davide adalamulira dziko lonse la Israele, ndipo ankayendetsa zonse mwachilungamo ndi mosakondera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Davide analamulira dziko lonse la Israeli ndipo ankachita zonse mwachilungamo ndi molondola pamaso pa anthu ake onse. Onani mutuwo |