2 Samueli 6:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo Mikala mwana wamkazi wa Saulo sanaone mwana kufikira tsiku la imfa yake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo Mikala mwana wamkazi wa Saulo sanaone mwana kufikira tsiku la imfa yake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Tsono Mikala, mwana wa Saulo, adaferamo osamuwona mwana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Ndipo Mikala mwana wa Sauli sanakhalenso ndi mwana mpaka anamwalira. Onani mutuwo |