Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 6:23 - Buku Lopatulika

23 Ndipo Mikala mwana wamkazi wa Saulo sanaone mwana kufikira tsiku la imfa yake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Ndipo Mikala mwana wamkazi wa Saulo sanaone mwana kufikira tsiku la imfa yake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Tsono Mikala, mwana wa Saulo, adaferamo osamuwona mwana.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Ndipo Mikala mwana wa Sauli sanakhalenso ndi mwana mpaka anamwalira.

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 6:23
9 Mawu Ofanana  

Ndipo ndidzaonjezanso kukhala ngati munthu woluluka, ndidzakhala wodzichepetsa m'maso a ine mwini; ndipo adzakazi udanenawo, ndi amenewo ndidzalemekezedwa.


Ndipo kunali pakukhala mfumuyo m'nyumba mwake, atampumulitsa Yehova pa adani ake onse omzungulira,


Ndipo Yehova wa makamu wadzivumbulutsa yekha m'makutu mwanga, Ndithu choipa chimenechi sichidzachotsedwa pa inu kufikira inu mudzafa, ati Ambuye, Yehova wa makamu.


Ndipo akazi asanu ndi awiri adzagwira mwamuna mmodzi tsiku limenelo, nati, Ife tidzadya chakudya chathuchathu ndi kuvala zovala zathuzathu; koma titchedwe dzina lako; chotsa chitonzo chathu.


Kunena za Efuremu, ulemerero wao udzauluka ndi kuchoka ngati mbalame; sipadzakhala kubala, ndi kukhala ndi pakati, ndi kuima.


ndipo sanamdziwe iye kufikira atabala mwana wake; namutcha dzina lake Yesu.


Ambuye wandichitira chotero m'masiku omwe Iye anandipenyera, kuchotsa manyazi anga pakati pa anthu.


Ndipo Samuele sanadzenso kudzaona Saulo kufikira tsiku la imfa yake; koma Samuele analira chifukwa cha Saulo; ndipo Yehova anali ndi chisoni kuti anamlonga Saulo mfumu ya Israele.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa