2 Samueli 6:21 - Buku Lopatulika21 Koma Davide ananena ndi Mikala, Ndatero pamaso pa Yehova, amene anandisankha ine ndi kupitirira atate wako ndi banja lake lonse, nandiika ndikhale mtsogoleri wa anthu a Yehova, wa Israele, chifukwa chake ndidzasewera pamaso pa Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Koma Davide ananena ndi Mikala, Ndatero pamaso pa Yehova, amene anandisankha ine ndi kupitirira atate wako ndi banja lake lonse, nandiika ndikhale mtsogoleri wa anthu a Yehova, wa Israele, chifukwa chake ndidzasewera pamaso pa Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Davide adamuyankha kuti, “Ndachita zimenezi molemekeza Chauta, amene adandisankhula ine kupambana bambo wako, ndiponso kupambana banja lonse la bambo wako. Ndipo adandiika kuti ndikhale mfumu ya Aisraele, anthu a Chauta. Choncho ndidzasangalalabe ndi kulemekeza Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Davide anamuyankha Mikala kuti, “Ndachita zimenezi molemekeza Yehova, amene anandisankha ine kupambana abambo ako, kapenanso kupambana banja la abambo ako. Ndipo anandisankha kuti ndikhale wolamulira Aisraeli, anthu a Yehova. Nʼchifukwa chake ndidzasangalalabe pamaso pa Yehova. Onani mutuwo |