Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 5:18 - Buku Lopatulika

18 Tsono Afilisti anafika natanda m'chigwa cha Refaimu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Tsono Afilisti anafika natanda m'chigwa cha Refaimu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Tsono Afilisti adabwera nakhala momwazikana m'chigwa cha Refaimu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Ndipo Afilisti anabwera ndi kukhala momwazika mʼChigwa cha Refaimu.

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 5:18
8 Mawu Ofanana  

Chaka chakhumi ndi chinai ndipo anadza Kedorilaomere ndi mafumu amene anali naye, nawakantha Arefaimu mu Asiteroti-Karanaimu, ndi Azuzimu mu Hamu, ndi Aemimu mu Savekiriyataimu,


Ndipo atatu a mwa makamu atatu opambanawo, anatsika nafika kwa Davide nyengo ya kukolola m'phanga la ku Adulamu; ndi gulu la Afilisti linamanga zithando m'chigwa cha Refaimu.


Ndipo Afilisti anakweranso kachiwiri, natanda m'chigwa cha Refaimu.


Ndipo atatu a akulu makumi atatu anatsikira kuthanthwe kwa Davide, ku phanga la Adulamu; ndi nkhondo ya Afilisti idamanga misasa m'chigwa cha Refaimu.


Ndipo padzakhala ngati wamasika alikumweta tirigu wosacheka, ndi dzanja lake lilikudula ngala; inde padzakhala ngati pamene wina akunkha ngala m'chigwa cha Refaimu.


nakwera malire kunka ku chigwa cha mwana wa Hinomu, kumbali kwa Ayebusi, kumwera, ndiko Yerusalemu; nakwera malire kunka kumwamba kwa phiri lokhala patsogolo pa chigwa cha Hinomu kumadzulo, ndilo ku mathero ake a chigwa cha Refaimu kumpoto.


Ndipo Yoswa ananena nao, Ngati muli anthu aunyinji, kwerani kuli mitengoko, ndi kudziswera minda m'dziko la Aperizi ndi la Arefaimu; akakucheperani malo kuphiri la Efuremu.


natsikira malire kunka polekezera phiri lokhala patsogolo pa chigwa cha mwana wa Hinomu, ndicho cha m'chigwa cha Refaimu kumpoto; natsikira ku chigwa cha Hinomu, ku mbali ya Ayebusi kumwera, natsikira ku Enirogele;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa