Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 5:17 - Buku Lopatulika

17 Koma pamene Afilisti anamva kuti adamdzoza Davide mfumu ya Israele, Afilisti onse anakwera kukafuna Davide; ndipo Davide anachimva natsikira kungaka kuja.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Koma pamene Afilisti anamva kuti adamdzoza Davide mfumu ya Israele, Afilisti onse anakwera kukafuna Davide; ndipo Davide anachimva natsikira kungaka kuja.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Afilisti atamva kuti Davide wadzozedwa kukhala mfumu yolamulira dziko la Aisraele, adapita kukamfunafuna. Koma Davide atamva zimenezo, adatsikira ku linga.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Afilisti atamva kuti Davide wadzozedwa kukhala mfumu ya Israeli, iwo anapita mwamphamvu kukamusakasaka. Koma Davide atamva zimenezi anakalowa mu linga.

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 5:17
11 Mawu Ofanana  

Ndipo Afilisti anaponyananso nkhondo ndi Aisraele; ndipo Davide anatsika ndi anyamata ake pamodzi naye naponyana ndi Afilisti; nafuna kukomoka Davide.


Pamenepo Davide anali m'linga, ndi boma la Afilisti linali mu Betelehemu.


ndi Elisama ndi Eliyada ndi Elifeleti.


Ndipo m'tsogolo mwake Davide anakantha Afilisti, nawagonjetsa Davide nalanda mudzi wa Metege Ama m'manja mwa Afilisti.


za Aaramu, za Amowabu, za ana a Amoni, za Afilisti, za Amaleke, ndi zofunkha za Hadadezere, mwana wa Rehobu mfumu ya ku Zoba.


Pamenepo Davide anali m'linga, ndi boma la asilikali a Afilisti linali ku Betelehemu.


amene mwa chikhulupiriro anagonjetsa maufumu, anachita chilungamo, analandira malonjezano, anatseka pakamwa pa mikango,


Tsono Afilisti anasonkhanitsa makamu ao onse ku Afeki; ndipo Aisraele anamanga ku chitsime cha mu Yezireele.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa