2 Samueli 3:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo iye sanakhoze kuyankha Abinere mau amodzi chifukwa cha kumuopa iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo iye sanakhoze kuyankha Abinere mau amodzi chifukwa cha kumuopa iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Pamenepo Isiboseti adangoti kukamwa yasa, osatha kumuyankha Abinere mau ndi amodzi omwe, chifukwa ankamuwopa kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Isiboseti sanayerekezenso kunena mawu ena kwa Abineri, chifukwa ankamuopa. Onani mutuwo |