2 Samueli 24:6 - Buku Lopatulika6 nafika ku Giliyadi ndi ku dera la Tatimuhodisi; nafika ku Dani-Yaana ndi kuzungulira, kufikira ku Sidoni, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 nafika ku Giliyadi ndi ku dera la Tatimuhodisi; nafika ku Dani-Yaana ndi kuzungulira, kufikira ku Sidoni, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Tsono adafika ku Giliyadi ndi ku Kadesi m'dziko la Ahiti, nakafika ku Dani, kuchokera kumeneko adayenda mozungulira ku Sidoni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Iwo anapita ku Giliyadi ndi ku chigwa cha Tahitimu Hodisi ndipo anapitirira mpaka ku Dani Yaani ndi madera ozungulira Sidoni. Onani mutuwo |