Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 23:11 - Buku Lopatulika

11 Ndipo wotsatana naye ndiye Sama mwana wa Age Muharari. Ndipo Afilisti anasonkhana ali gulu pa Lehi pamene panali munda wamphodza; anthu nathawa Afilistiwo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Ndipo wotsatana naye ndiye Sama mwana wa Age Muharari. Ndipo Afilisti anasonkhana ali gulu pa Lehi pamene panali munda wamphodza; anthu nathawa Afilistiwo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Wotsatana ndi ameneyo anali Sama, mwana wa Age Muharari. Nthaŵi ina Afilisti adasonkhana ku Lehi kumene kunali munda wa mphodza. Aisraele nkuthaŵa Afilisti aja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Wotsatana naye anali Sama mwana wa Age Mharari. Pamene Afilisti anasonkhana pamalo pamene panali munda wa mphodza, ankhondo a Israeli anathawa Afilistiwo.

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 23:11
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Yakobo anampatsa Esau mkate ndi mphodza zophika; ndipo iye anadya, namwa, nanyamuka, napita: chomwecho Esau ananyoza ukulu wake.


Sama Muharari, Ahiyamu mwana wa Sarara Muharari;


Samoti Muharodi, Helezi Mpeloni,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa