2 Samueli 22:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo Davide analankhula kwa Yehova mau a nyimbo iyi tsikuli Yehova anampulumutsa m'dzanja la adani ake onse, ndi m'dzanja la Saulo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo Davide analankhula kwa Yehova mau a nyimbo iyi tsikuli Yehova anampulumutsa m'dzanja la adani ake onse, ndi m'dzanja la Saulo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Tsiku limene Chauta adaapulumutsa Davide kwa adani ake onse ndiponso kwa Saulo, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Davide anayimbira Yehova nyimbo iyi pamene Yehovayo anamupulumutsa mʼdzanja la adani ake onse ndiponso mʼdzanja la Sauli. Onani mutuwo |