2 Samueli 21:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo anauza Davide chimene Rizipa mwana wamkazi wa Aya, mkazi wamng'ono wa Saulo anachita. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo anauza Davide chimene Rizipa mwana wamkazi wa Aya, mkazi wamng'ono wa Saulo anachita. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Davide atamva zimene Rizipa mwana wa Aya, mzikazi wa Saulo adachita, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Davide atawuzidwa zimene Rizipa mwana wamkazi wa Ayiwa, mzikazi wa Sauli anachita, Onani mutuwo |