2 Samueli 20:5 - Buku Lopatulika5 Chomwecho Amasa anamuka kukaitana anthu a Yuda asonkhane; koma anachedwa, napitiriza nthawi imene idamuikira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Chomwecho Amasa anamuka kukaitana anthu a Yuda asonkhane; koma anachedwa, napitiriza nthawi imene idamuikira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Motero Amasa adakaitana Ayuda. Koma adachedwa, napitiriza nthaŵi imene adaamuikira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Motero Amasa anakayitana Ayuda, koma anachedwa, napitirira pa nthawi imene mfumu inamuyikira. Onani mutuwo |