2 Samueli 20:4 - Buku Lopatulika4 Pamenepo mfumu inati kwa Amasa, Undiitanire anthu a Yuda asonkhane asanapite masiku atatu, nukhale pano iwenso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Pamenepo mfumu inati kwa Amasa, Undiitanire anthu a Yuda asonkhane asanapite masiku atatu, nukhale pano iwenso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Tsono mfumu idauza Amasa kuti, “Itanire anthu onse a ku Yuda, abwere kuno pasanapite masiku atatu, ndipo iweyo udzakhalepo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Kenaka mfumu inati kwa Amasa, “Itanitsa ankhondo a Yuda kuti abwere kwa ine pasanathe masiku atatu, ndipo iwe udzakhale nawo.” Onani mutuwo |