2 Samueli 2:27 - Buku Lopatulika27 Yowabu nati, Pali Mulungu, iwe ukadapanda kunena, anthu akadabalalika m'mawa osatsata yense mbale wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Yowabu nati, Pali Mulungu, iwe ukadapanda kunena, anthu akadabalalika m'mawa osatsata yense mbale wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Yowabu adayankha kuti, “Ndithudi, ndikulumbira, pali Mulungu wamoyo, ukadapanda kulankhula, ankhondo angaŵa sakadaleka kuŵathamangitsa abale aowo mpaka maŵa m'maŵa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Yowabu anayankha kuti, “Pali Yehova wamoyo, ukanapanda kuyankhula, ankhondo anga akanapitiriza kuthamangitsa abale awo mpaka mmawa.” Onani mutuwo |