Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 2:20 - Buku Lopatulika

20 Pomwepo Abinere anacheuka nati, Kodi ndi iwe Asahele? Iye nayankha, Ndine.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Pomwepo Abinere anacheuka nati, Kodi ndi iwe Asahele? Iye nayankha, Ndine.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Tsono Abinere adacheuka nati, “Kodi ndiwe, Asahele?” Iye adayankha kuti, “Ndine amene.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Abineri anayangʼana mʼmbuyo ndipo anafunsa, “Kodi ndiwe Asaheli?” Iye anayankha kuti, “Ndine.”

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 2:20
2 Mawu Ofanana  

Ndipo Asahele anapirikitsa Abinere. Ndipo m'kuthamanga kwake sanapatukire kulamanja, kapena kulamanzere, pakutsata Abinere.


Ndipo Abinere ananena naye, Patuka iwe kulamanja kapena kulamanzere kwako nudzigwirire wina wa anyamatawo, nutenge zida zake. Koma Asahele anakana kupatuka pakumtsata iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa