2 Samueli 2:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo Abinere mwana wa Nere ndi anyamata a Isiboseti mwana wa Saulo anatuluka ku Mahanaimu kunka ku Gibiyoni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo Abinere mwana wa Nere ndi anyamata a Isiboseti mwana wa Saulo anatuluka ku Mahanaimu kunka ku Gibiyoni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Tsono Abinere mwana wa Nere pamodzi ndi ankhondo a Isiboseti mwana wa Saulo adapita ku Gibiyoni kuchokera ku Mahanaimu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Abineri mwana wa Neri, pamodzi ndi ankhondo a Isi-Boseti mwana wa Sauli, anachoka ku Mahanaimu ndi kupita ku Gibiyoni. Onani mutuwo |