2 Samueli 19:43 - Buku Lopatulika43 Ndipo anthu a Israele anayankha anthu a Yuda, nati, Ife tili ndi magawo khumi mwa mfumu, ndi mwa Davide koposa inu; chifukwa ninji tsono munatipeputsa ife, osayamba kupangana nafe za kubwezanso mfumu yathu? Koma mau a anthu a Yuda anali aukali koposa mau a anthu a Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201443 Ndipo anthu a Israele anayankha anthu a Yuda, nati, Ife tili ndi magawo khumi mwa mfumu, ndi mwa Davide koposa inu; chifukwa ninji tsono munatipeputsa ife, osayamba kupangana nafe za kubwezanso mfumu yathu? Koma mau a anthu a Yuda anali aukali koposa mau a anthu a Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa43 Apo Aisraelewo adayankha Ayuda aja kuti, “Tili ndi zigawo khumi mwa mfumu imeneyi, ndipo mwa ufumu wa Davide ife tili ndi zigawo zambiri kupambana inu. Nanga chifukwa chiyani tsono mukutinyoza? Kodi ife sindife amene tidayamba kulankhula zoti mfumu yathu ibwerenso?” Koma anthu a ku Yuda adalankhula mwaukali kwambiri kupambana anthu a ku Israele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero43 Aisraeli anayankha Ayuda kuti, “Ife ndi magawo khumi mwa mfumu imeneyi, ndipo kuwonjezera apo, ife tili ndi zinthu zambiri mwa Davide kuposa inu. Tsono nʼchifukwa chiyani mukutichita chipongwe? Kodi ife si amene tinayamba kunena za kubweretsa mfumu yathu?” Koma anthu a Yuda anayankha mwaukali kwambiri kupambana anthu a ku Israeli. Onani mutuwo |